Yeremiya 40:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Yeremiya ananka kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa, nakhala kumeneko kwa anthu otsala m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Yeremiya ananka kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa, nakhala kumeneko kwa anthu otsala m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamenepo Yeremiya adapita kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa. Ndipo adakhala naye pakati pa anthu otsala m'dzikomo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Motero Yeremiya anapita kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa ndipo anakakhala naye kumeneko pakati pa anthu amene anatsala mʼdzikomo. Onani mutuwo |