Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 40:16 - Buku Lopatulika

16 Koma Gedaliya mwana wa Ahikamu anati kwa Yohanani mwana wa Kareya, Usachite ichi; pakuti unamizira Ismaele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma Gedaliya mwana wa Ahikamu anati kwa Yohanani mwana wa Kareya, Usachite ichi; pakuti unamizira Ismaele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma Gedaliya mwana wa Ahikamu adayankha Yohanani mwana wa Kareya kuti, “Iyai, usachite zotero. Zimene ukunena za Ismaele nzabodza.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Koma Gedaliya mwana wa Ahikamu anawuza Yohanani mwana wa Kareya kuti, “Usachite zimenezo! Zimene ukunena za Ismaeli ndi zabodza.”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 40:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anauka Ismaele mwana wa Netaniya, ndi anthu khumi okhala naye, namkantha Gedaliya mwana wa Ahikamu mwana wa Safani ndi lupanga, namupha iye, amene mfumu ya ku Babiloni inamuika wolamulira dziko.


Ndipo tilekerenji kunena, Tichite zoipa kuti zabwino zikadze (monganso ena atinamiza ndi kuti timanena)? Kulanga kwa amenewo kuli kolungama.


sichichita zosayenera, sichitsata za mwini yekha, sichipsa mtima, sichilingirira zoipa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa