Yeremiya 40:13 - Buku Lopatulika13 Ndiponso Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala m'minda, anadza kwa Gedaliya ku Mizipa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndiponso Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala m'minda, anadza kwa Gedaliya ku Mizipa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Tsiku lina Yohanani mwana wa Kareya, pamodzi ndi atsogoleri ankhondo amene sadadzipereke aja, adapita kwa Gedaliya ku Mizipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri a ankhondo onse amene sanadzipereke aja anabwera ku Mizipa kwa Gedaliya Onani mutuwo |