Yeremiya 4:28 - Buku Lopatulika28 Chifukwa chimenecho dziko lidzalira maliro, ndipo kumwamba kudzada; chifukwa ndanena, ndatsimikiza mtima, sindinatembenuka, sindidzabwerera pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Chifukwa chimenecho dziko lidzalira maliro, ndipo kumwamba kudzada; chifukwa ndanena, ndatsimikiza mtima, sindinatembenuka, sindidzabwerera pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Chifukwa cha zimenezi dziko lonse lapansi lidzalira ndipo zakumwamba zidzachita mdima. Pakuti Ine ndalankhula, ndipo ndili ndi cholinga. Sindidafeŵe mtima, ndipo sindidzabwerera konse m'mbuyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Chifukwa chake dziko lapansi lidzalira ndipo thambo lidzachita mdima, pakuti ndayankhula ndipo sindidzafewa mtima, ndatsimikiza ndipo sindidzabwerera mʼmbuyo.” Onani mutuwo |