Yeremiya 4:27 - Buku Lopatulika27 Pakuti Yehova atero, Dziko lonse lidzakhala bwinja koma sindidzatsirizitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Pakuti Yehova atero, Dziko lonse lidzakhala bwinja koma sindidzatsirizitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Chauta akunena kuti, “Dziko lonse lidzasanduka chipululu, komabe sindidzaliwononga kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Yehova akuti, “Dziko lonse lidzasanduka chipululu komabe sindidzaliwononga kotheratu. Onani mutuwo |