Yeremiya 4:26 - Buku Lopatulika26 Ndinaona, ndipo taona, munda wazipatso unali chipululu, ndipo mizinda yake yonse inapasuka pamaso pa Yehova, ndi pamaso pa mkwiyo wake woopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndinaona, ndipo taona, munda wazipatso unali chipululu, ndipo midzi yake yonse inapasuka pamaso pa Yehova, ndi pamaso pa mkwiyo wake woopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndidayang'ana, dziko la chonde linali litasanduka chipululu, mizinda yake yonse inali itasanduka mabwinja, chifukwa cha mkwiyo wa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ndinayangʼana, dziko lachonde linali litasanduka chipululu; mizinda yake yonse inali itasanduka bwinja pamaso pa Yehova, chifukwa cha mkwiyo wake. Onani mutuwo |