Yeremiya 4:25 - Buku Lopatulika25 Ndinaona, ndipo taona, panalibe munthu, ndi mbalame zonse zakumwamba zinathawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndinaona, ndipo taona, panalibe munthu, ndi mbalame zonse zakumwamba zinathawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndidayang'ana, osaona ndi munthu mmodzi yemwe, ndipo mbalame zonse zamumlengalenga zinali zitathaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ndinayangʼana, ndipo sindinaone anthu; mbalame iliyonse ya mlengalenga inali itathawa. Onani mutuwo |