Yeremiya 4:23 - Buku Lopatulika23 Ndinaona dziko lapansi, ndipo taona, linali lopasuka lopanda kanthu; ndipo ndinaona kumwamba, kunalibe kuunika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndinaona dziko lapansi, ndipo taona, linali lopasuka lopanda kanthu; ndipo ndinaona kumwamba, kunalibe kuunika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndidayang'ana dziko lapansi, linali lopanda anthu ndi lopanda kanthu kalikonse. Ndidayang'ana thambo, linalibe konse kuŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndinayangʼana dziko lapansi, ndipo linali lopanda anthu ndi lopanda kanthu; ndinayangʼana thambo, koma linalibe kuwala kulikonse. Onani mutuwo |