Yeremiya 4:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti anthu anga apusa, sandidziwa Ine; ali ana opulukira sazindikira; ali ochenjera kuchita choipa koma kuchita chabwino sakudziwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti anthu anga apusa, sandidziwa Ine; ali ana opulukira sazindikira; ali ochenjera kuchita choipa koma kuchita chabwino sakudziwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Chauta akuti “Paja anthu anga ndi opusa, Ine sandidziŵa. Ali ngati ana opulukira, osamvetsa chilichonse. Ali ndi luso pochita zoipa, koma kuchita zabwino sadziŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Yehova akuti, “Anthu anga ndi zitsiru; iwo sandidziwa. Iwo ndi ana opanda nzeru; samvetsa chilichonse. Ali ndi luso lochita zoyipa, koma sadziwa kuchita zabwino.” Onani mutuwo |