Yeremiya 4:21 - Buku Lopatulika21 Kufikira liti ndidzaona mbendera, ndi kumva kulira kwa lipenga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Kufikira liti ndidzaona mbendera, ndi kumva kulira kwa lipenga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Kodi ndikhale ndikuwona mbendera yankhondo mpaka liti? Kodi ndikhale ndikumva lipenga mpaka liti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kodi ndikhale ndikuona mbendera ya nkhondo, ndi kumva kulira kwa lipenga mpaka liti? Onani mutuwo |