Yeremiya 4:20 - Buku Lopatulika20 Alalikira chipasuko chilalikire; pakuti dziko lonse lafunkhidwa; mahema anga afunkhidwa dzidzidzi, ndi nsalu zanga zotchinga m'kamphindi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Alalikira chipasuko chilalikire; pakuti dziko lonse lafunkhidwa; mahema anga afunkhidwa dzidzidzi, ndi nsalu zanga zotchinga m'kamphindi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tsoka limatsata tsoka linzake, ndipo dziko lonse lasanduka bwinja. Mwadzidzidzi mahema athu aonongeka, machinga ake agwetsedwa pa kanthaŵi kang'onong'ono. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tsoka limatsata tsoka linzake; dziko lonse lasanduka bwinja. Mwadzidzidzi matenti athu awonongedwa, mwa kanthawi kochepa nsalu zake zotchinga zagwetsedwa. Onani mutuwo |