Yeremiya 4:14 - Buku Lopatulika14 Iwe Yerusalemu, utsuke mtima wako kuchotsa zoipa kuti upulumuke. Maganizo ako achabe agona mwako masiku angati? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Iwe Yerusalemu, utsuke mtima wako kuchotsa zoipa kuti upulumuke. Maganizo ako achabe agona mwako masiku angati? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Iwe Yerusalemu, chotsa zoipa mumtima mwako kuti upulumuke. Kodi maganizo ako oipa udzakhala nawobe mpaka liti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iwe Yerusalemu, tsuka mtima wako kuchotsa zoyipa kuti upulumuke. Kodi maganizo ako oyipawo udzakhala nawo mpaka liti? Onani mutuwo |