Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 39:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo anakolowola maso a Zedekiya, nammanga m'zigologolo, kunka naye ku Babiloni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo anakolowola maso a Zedekiya, nammanga m'zigologolo, kunka naye ku Babiloni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Kenaka idamkolowola maso Zedekiyayo, nimmanga ndi maunyolo nkupita naye ku Babiloni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kenaka inakolowola maso a Zedekiya ndi kumumanga ndi maunyolo a mkuwa nʼkupita naye ku Babuloni.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 39:7
10 Mawu Ofanana  

Napha ana a Zedekiya pamaso pake, namkolowola Zedekiya maso ake, nammanga ndi maunyolo amkuwa, namuka naye ku Babiloni.


Ndidzasamalira malemba anu: Musandisiye ndithu.


Pakuti Yehova atero, Taonani, ndidzakuyesa iwe choopsa cha kwa iwe mwini, ndi kwa abwenzi ako onse; ndipo iwo adzagwa ndi lupanga la adani ao, ndipo maso ako adzaona; ndipo ndidzapereka Ayuda onse m'dzanja la mfumu ya ku Babiloni, ndipo iye adzawatengera iwo am'nsinga ku Babiloni, nadzawapha ndi lupanga.


ndipo iwe sudzapulumuka m'dzanja lake, koma udzagwiridwadi, nudzaperekedwa m'dzanja lake; ndipo maso ako adzaonana nao a mfumu ya ku Babiloni, ndipo iye adzanena nawe pakamwa ndi pakamwa, ndipo udzanka ku Babiloni.


Yehova atero: Taonani, ndidzapereka Farao Hofira mfumu ya Aejipito m'manja a adani ake, ndi m'manja a iwo akufuna moyo wake; monga ndinapereka Zedekiya mfumu ya Yuda m'manja a Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni mdani wake, amene anafuna moyo wake.


Ndipo anakolowola maso a Zedekiya, ndipo mfumu ya ku Babiloni inammanga m'zigologolo, nimtengera ku Babiloni, nimuika m'ndende mpaka tsiku la kufa kwake.


Ndidzamphimba ndi ukonde wanga, nadzakodwa iye mu msampha wanga; ndipo ndidzafika naye ku Babiloni, ku dziko la Ababiloni; sadzaliona, chinkana adzafako.


Pamenepo Afilisti anamgwira, namkolowola maso, natsika naye ku Gaza, nammanga ndi maunyolo amkuwa; namperetsa m'kaidi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa