Yeremiya 39:2 - Buku Lopatulika2 Chaka chakhumi ndi chimodzi cha Zedekiya, mwezi wachinai, tsiku lachisanu ndi chinai, mzinda unabooledwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chaka chakhumi ndi chimodzi cha Zedekiya, mwezi wachinai, tsiku lachisanu ndi chinai, mudzi unabooledwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pa chaka chakhumi ndi chimodzi cha ufumu wa Zedekiya, mwezi wachinai, tsiku lachisanu ndi chinai la mweziwo, malinga a mzindawo adabooledwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo pa tsiku lachisanu ndi chinayi la mwezi wachinayi wa chaka cha khumi ndi chimodzi cha Zedekiya, malinga a mzindawo anabowoledwa. Onani mutuwo |