Yeremiya 39:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yeremiya, potsekeredwa iye m'bwalo la kaidi, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yeremiya, potsekeredwa iye m'bwalo la kaidi, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Chauta adalankhula ndi Yeremiya pamene anali m'ndende ku bwalo la alonda. Adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Yeremiya ali mʼndende ku bwalo la alonda, Yehova anayankhula naye: Onani mutuwo |