Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 39:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yeremiya, potsekeredwa iye m'bwalo la kaidi, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yeremiya, potsekeredwa iye m'bwalo la kaidi, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Chauta adalankhula ndi Yeremiya pamene anali m'ndende ku bwalo la alonda. Adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Yeremiya ali mʼndende ku bwalo la alonda, Yehova anayankhula naye:

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 39:15
8 Mawu Ofanana  

Ndipo akulu anakwiyira Yeremiya, nampanda iye, namuika m'nyumba yandende m'nyumba ya Yonatani mlembi; pakuti anaiyesa ndende.


Ndipo Zedekiya mfumu analamula, ndipo anamuika Yeremiya m'bwalo la kaidi, tsiku ndi tsiku, nampatsa mkate wofuma kumseu wa oumba mikate, mpaka unatha mkate wonse wa m'mzinda. Ndipo Yeremiya anakhala m'bwalo la kaidi.


Ndipo anamkweza Yeremiya ndi zingwe, namtulutsa m'dzenjemo; ndipo Yeremiya anakhalabe m'bwalo la kaidi.


Ndipo Yeremiya anakhala m'bwalo la kaidi mpaka tsiku lakugwidwa Yerusalemu. Ndipo anali komweko pogwidwa Yerusalemu.


iwonso anatumiza, namchotsa Yeremiya m'bwalo la kaidi, nampereka iye kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu, mwana wa Safani, kuti anke naye kwao; momwemo iye anakhala ndi anthu.


m'menemo ndimva zowawa kufikira zomangira, monga wochita zoipa; koma mau a Mulungu samangika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa