Yeremiya 39:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni anamuuza Nebuzaradani kapitao wa alonda, za Yeremiya, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni anamuuza Nebuzaradani kapitao wa alonda, za Yeremiya, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nebukadinezara, mfumu ya ku Babiloni, adatumiza mau kwa Nebuzaradani mtsogoleri wa alonda ankhondo, onena za Yeremiya. Adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tsono Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni inatuma mawu kwa Nebuzaradani mtsogoleri wa alonda ankhondo a mfumu za Yeremiya. Iye anati: Onani mutuwo |