Yeremiya 38:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo mfumu Zedekiya anati, Taonani, ali m'manja mwanu; pakuti mfumu singathe kuchita kanthu kotsutsana nanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo mfumu Zedekiya anati, Taonani, ali m'manja mwanu; pakuti mfumu singathe kuchita kanthu kotsutsana nanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mfumu Zedekiya adati, “Suyu, ali m'manja mwanu. Ine mfumu sindingakuletseni ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mfumu Zedekiya anayankha kuti, “Munthuyu ali mʼmanja mwanu. Ine sindingakuletseni chimene mukufuna kumuchitira.” Onani mutuwo |