Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 38:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo Zedekiya anati kwa Yeremiya, Anthu asadziwe mau amene, ndipo sudzafa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo Zedekiya anati kwa Yeremiya, Anthu asadziwe mau amene, ndipo sudzafa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Pamenepo Zedekiya adauza Yeremiya kuti, “Usauze munthu wina aliyensetu zimenezi, kuti ungaphedwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Pamenepo Zedekiya anati kwa Yeremiya, “Usawuze munthu wina aliyense zimene takambiranazi, ukatero udzaphedwa.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 38:24
3 Mawu Ofanana  

pamenepo Zedekiya mfumu inatuma, ndi kumtenga iye; ndipo mfumu inamfunsa iye m'tseri m'nyumba mwake, niti, Kodi alipo mau ochokera kwa Yehova? Ndipo Yeremiya, anati, Alipo. Anatinso, Mudzaperekedwa m'dzanja la mfumu ya ku Babiloni.


Ndipo adzatulutsira Ababiloni akazi anu onse, ndi ana anu, ndipo simudzapulumuka m'manja ao, koma mudzagwidwa ndi dzanja la mfumu ya ku Babiloni; ndipo mudzatenthetsa mzindawu ndi moto.


Koma akamva akulu kuti ndalankhula ndi iwe, nakafika kwa iwe, ndi kuti kwa iwe, Utifotokozere ife chomwe wanena kwa mfumu; osatibisira ichi, ndipo sitidzakupha iwe; ndiponso zomwe mfumu inanena kwa iwe;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa