Yeremiya 38:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo adzatulutsira Ababiloni akazi anu onse, ndi ana anu, ndipo simudzapulumuka m'manja ao, koma mudzagwidwa ndi dzanja la mfumu ya ku Babiloni; ndipo mudzatenthetsa mzindawu ndi moto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo adzatulutsira Ababiloni akazi anu onse, ndi ana anu, ndipo simudzapulumuka m'manja ao, koma mudzagwidwa ndi dzanja la mfumu ya ku Babiloni; ndipo mudzatenthetsa mudziwu ndi moto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Akazi anu onse pamodzi ndi ana adzaŵapereka m'manja mwa Ababiloni. Ndipo inuinuyo simudzalephera kugwa m'manja mwao. Mudzagwidwa ndi mfumu ya ku Babiloni, kenaka mzinda uno adzautentha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 “Akazi pamodzi ndi ana anu adzaperekedwa kwa Ababuloni. Inuyo simudzapulumuka mʼmanja mwawo koma mfumu ya ku Babuloni idzakugwirani; mzinda uno adzawutentha.” Onani mutuwo |