Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 38:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Ebedemeleki Mkusi anati kwa Yeremiya, Kulungatu zingwe ndi nsaluzi zotaya zakale ndi zansanza ndi kuzikwapatira. Ndipo Yeremiya anachita chomwecho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Ebedemeleki Mkusi anati kwa Yeremiya, Kulungatu zingwe ndi nsaluzi zotaya zakale ndi zansanza ndi kuzikwapatira. Ndipo Yeremiya anachita chomwecho.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Ebedemeleki Mkusi uja adauza Yeremiya kuti, “Ikani nsanzazi m'kwapa mwanu kuti zingwe zingakupwetekeni.” Yeremiya adachitadi zimenezo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ebedi-Meleki, Mkusi, anawuza Yeremiya kuti, “Ika sanzazo mkwapa mwako kuti zingwe zingakupweteke.” Yeremiya anachitadi zimenezi,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 38:12
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Ebedemeleki anatenga anthuwo, nalowa nao m'nyumba ya mfumu ya pansi pa nyumba ya chuma, natenga m'menemo nsalu zakale zotaya ndi zansanza zovunda, nazitsitsira ndi zingwe kwa Yeremiya m'dzenjemo.


Ndipo anamkweza Yeremiya ndi zingwe, namtulutsa m'dzenjemo; ndipo Yeremiya anakhalabe m'bwalo la kaidi.


Ndipo pamene Ebedemeleki Mkusi, mdindo, anamva kuti anamuika Yeremiya m'dzenje; mfumu ilikukhala pa Chipata cha Benjamini;


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


Kondwani nao iwo akukondwera; lirani nao akulira.


Koma mukhalirane okoma wina ndi mnzake, a mtima wachifundo, akukhululukirana nokha, monganso Mulungu mwa Khristu anakhululukira inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa