Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 37:9 - Buku Lopatulika

9 Yehova atero: Musadzinyenge, kuti, Ababiloni adzatichokera ndithu; pakuti sadzachoka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Yehova atero: Musadzinyenge, kuti, Ababiloni adzatichokera ndithu; pakuti sadzachoka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Zimene akunena Chauta ndi izi, akuti musadzinyenge ndi kumaganiza kuti Ababiloni adzachoka ndi kukusiyani. Pepani sadzachoka ai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Yehova akuti: Musadzinyenge, nʼkumaganiza kuti, ‘Ndithu Ababuloni adzatisiya.’ Ndithudi sadzakusiyani!

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 37:9
9 Mawu Ofanana  

Asatame zopanda pake, kudzinyenga nazo; pakuti zopanda pake zidzakhala chombwezera chake.


Pakuti Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero: Aneneri anu ndi akuombeza anu amene akhala pakati panu, asakunyengeni inu, musamvere maloto anu amene mulotetsa.


Kudzikuza kwa mtima wako kwakunyenga, iwe wokhala m'mapanga a thanthwe, iwe pokhala pako pamwamba, wakunena m'mtima mwake, Adzanditsitsira pansi ndani?


Pakuti ngati wina ayesa ali kanthu pokhala ali chabe, adzinyenga yekha.


Musanyengedwe; Mulungu sanyozeka; pakuti chimene munthu achifesa, chimenenso adzachituta.


Asakunyengeni inu munthu ndi mau opanda pake, pakuti chifukwa cha izi umadza mkwiyo wa Mulungu pa ana a kusamvera.


munthu asakunyengeni konseko; kuti silifika, koma chiyambe chafika chipatukocho, navumbulutsike munthu wosaweruzika, mwana wa chionongeko,


Khalani akuchita mau, osati akumva okha, ndi kudzinyenga nokha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa