Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 37:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Yeremiya analikuyendayenda mwa anthu; chifukwa sanamuike iye m'nyumba yandende.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Yeremiya analikuyendayenda mwa anthu; chifukwa asanamuike iye m'nyumba yandende.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Pa nthaŵi imeneyo nkuti Yeremiya asanaponyedwe m'ndende, choncho anali ndi ufulu wotha kuyenda pakati pa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Nthawi imeneyinso nʼkuti Yeremiya ali ndi ufulu woyenda pakati pa anthu chifukwa anali asanaponyedwe mʼndende.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 37:4
2 Mawu Ofanana  

Ndipo akulu anakwiyira Yeremiya, nampanda iye, namuika m'nyumba yandende m'nyumba ya Yonatani mlembi; pakuti anaiyesa ndende.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa