Yeremiya 37:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Zedekiya mfumu anatuma Yehukala mwana wa Selemiya, ndi Zefaniya mwana wa Maaseiya wansembe, kwa Yeremiya mneneri, kukanena, Mutipemphereretu kwa Yehova Mulungu wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Zedekiya mfumu anatuma Yehukala mwana wa Selemiya, ndi Zefaniya mwana wa Maaseiya wansembe, kwa Yeremiya mneneri, kukanena, Mutipemphereretu kwa Yehova Mulungu wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono mfumu Zedekiya adatuma Yehukala, mwana wa Semaliya ndi wansembe Zefaniya, mwana wa Maseiya, kwa mneneri Yeremiya kukamuuza kuti, “Mutipempherere kwa Chauta, Mulungu wathu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono Zedekiya anatuma Yehukali mwana wa Selemiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa mneneri Yeremiya ndi uthenga uwu: “Chonde tipempherereni kwa Yehova Mulungu wathu.” Onani mutuwo |