Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 37:16 - Buku Lopatulika

16 Atafika Yeremiya kunyumba yadzenje, ku tizipinda take nakhalako Yeremiya masiku ambiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Atafika Yeremiya kunyumba yadzenje, ku tizipinda take nakhalako Yeremiya masiku ambiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Yeremiya adaikidwa m'ndende ya pansi pa nthaka, nakhala m'menemo nthaŵi yaitali.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Yeremiya anayikidwa mʼndende ya pansi pa nthaka, kumene anakhalako nthawi yayitali.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 37:16
5 Mawu Ofanana  

chifukwa kuti ndinabedwa ndithu m'dziko la Ahebri; ndiponso pano sindinachite kanthu kakundiikira ine m'dzenjemu.


Ndipo anatenga Yeremiya, namponya iye m'dzenje la Malikiya mwana wake wa mfumu, limene linali m'bwalo la kaidi; ndipo anamtsitsa Yeremiya ndi zingwe. Koma m'dzenjemo munalibe madzi, koma thope; namira Yeremiya m'thopemo.


anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwamba pa ine;


Ndinaitana dzina lanu, Yehova, ndili m'dzenje lapansi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa