Yeremiya 36:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Baruki mwana wa Neriya anachita monga mwa zonse anamuuza iye Yeremiya mneneri, nawerenga m'buku mau a Yehova m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Baruki mwana wa Neriya anachita monga mwa zonse anamuuza iye Yeremiya mneneri, nawerenga m'buku mau a Yehova m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Motero Baruki mwana wa Neriya adachita zonse zimene mneneri Yeremiya adamuuza kuti achite. Adaŵerenga mau a Chauta olembedwa m'buku aja m'Nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Baruki mwana wa Neriya anachita zonse zimene mneneri Yeremiya anamuwuza kuti achite. Mʼnyumba ya Yehova, iye anawerenga mawu a Yehova ochokera mʼbukulo. Onani mutuwo |