Yeremiya 36:3 - Buku Lopatulika3 Kapena nyumba ya Yuda idzamva choipa chonse chimene nditi ndidzawachitire; kuti abwerere yense kuleka njira yake yoipa; kuti ndikhululukire mphulupulu yao ndi tchimo lao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kapena nyumba ya Yuda idzamva choipa chonse chimene nditi ndidzawachitire; kuti abwerere yense kuleka njira yake yoipa; kuti ndikhululukire mphulupulu yao ndi tchimo lao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mwina mwake banja la Yuda lidzamva za zoopsa zonse zimene ndikuti ndiŵagwetsere. Choncho munthu aliyense adzasiya makhalidwe ake oipa. Motero ndidzaŵakhululukira zolakwa zao ndi machimo ao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mwina mwake anthu a ku Yuda adzamva za zoopsa zonse zimene ndakonza kuti ndiwachitire, ndipo munthu aliyense adzatembenuka ndi kusiya ntchito zake zoyipa. Motero ndidzawakhululukira zoyipa zawo ndi machimo awo.” Onani mutuwo |