Yeremiya 34:4 - Buku Lopatulika4 Koma tamva mau a Yehova, iwe Zedekiya mfumu ya Yuda; Yehova atero za iwe, Sudzafa ndi lupanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma tamva mau a Yehova, iwe Zedekiya mfumu ya Yuda; Yehova atero za iwe, Sudzafa ndi lupanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Komabe imva mau a Chauta, iwe Zedekiya mfumu ya ku Yuda. Akuti, Sudzafera pa nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Koma iwe Zedekiya mfumu ya Yuda, imva lonjezo ili la Yehova. Izi ndi zimene Yehova akunena za iwe: Sudzaphedwa pa nkhondo; Onani mutuwo |