Yeremiya 33:2 - Buku Lopatulika2 Atero Yehova wochita zake, Yehova wolenga zake kuti azikhazikitse; dzina lake ndi Yehova: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Atero Yehova wochita zake, Yehova wolenga zake kuti azikhazikitse; dzina lake ndi Yehova: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Naŵa mau a Chauta amene adalenga dziko lapansi, naliwumba ndi kulikhazikitsa. Iyeyo dzina lakedi ndi Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Yehova amene analenga dziko lapansi, kuliwumba ndi kulikhazikitsa; amene dzina lake ndi Yehova, akuti, Onani mutuwo |