Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 32:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Yeremiya anati, Mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Yeremiya anati, Mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Yeremiya adanena kuti, “Chauta adandiwuza kuti

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Yeremiya anati, “Yehova wandiwuza kuti:

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 32:6
3 Mawu Ofanana  

Arauna nati, Mbuye wanga mfumu, mwadzeranji kwa mnyamata wanu? Ndipo Davide, anati, Kugula dwale lako ili, kuti ndimangirepo Yehova guwa la nsembe, kuti mliriwo ulekeke kwa anthu.


ndipo adzatsogolera Zedekiya kunka ku Babiloni, ndipo adzakhala komweko kufikira ndidzamzonda, ati Yehova: ngakhale mudzamenyana ndi Ababiloni, simudzapindula konse?


Taonani, Hanamele mwana wa Salumu mbale wa atate wako adzadza kwa iwe, kuti, Ugule munda wanga uli ku Anatoti; pakuti mphamvu yakuombola ndi yako kuugula.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa