Yeremiya 32:36 - Buku Lopatulika36 Chifukwa chake tsopano atero Yehova, Mulungu wa Israele, za mzinda umene, munena inu, waperekedwa m'dzanja la mfumu ya Babiloni ndi lupanga, ndi njala, ndi mliri: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Chifukwa chake tsopano atero Yehova, Mulungu wa Israele, za mudzi umene, munena inu, waperekedwa m'dzanja la mfumu ya Babiloni ndi lupanga, ndi njala, ndi chaola: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Anthu ponena za mzinda umenewu akuti udzaperekedwa kwa mfumu ya ku Babiloni utafooka ndi nkhondo, njala ndi mliri. Komatu zimene Chauta, Mulungu wa Israele akunena ndi izi: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 “Anthu ponena za mzindawu akuti udzaperekedwa kwa mfumu ya ku Babuloni mwa nkhondo, njala ndi mliri, koma Yehova Mulungu wa Israeli akuti, Onani mutuwo |