Yeremiya 32:34 - Buku Lopatulika34 Koma anaika zonyansa zao m'nyumba yotchedwa dzina langa, kuti aidetse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Koma anaika zonyansa zao m'nyumba yotchedwa dzina langa, kuti aidetse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Adaika mafano ao onyansa m'Nyumba imene imadziŵika ndi dzina langa, ndipo adaiipitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iwo anayika mafano awo onyansa mʼnyumba imene imadziwika ndi dzina langa ndipo anayipitsa. Onani mutuwo |