Yeremiya 32:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo Inu Yehova Mulungu mwati kwa ine, Udzigulire munda ndi ndalama, nuitane mboni; koma mzinda waperekedwa m'manja a Ababiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo Inu Yehova Mulungu mwati kwa ine, Udzigulire munda ndi ndalama, nuitane mboni; koma mudzi waperekedwa m'manja a Ababiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Komabe ngakhale mzindawu udzaperekedwa kwa Ababiloni, Inu Chauta mudandilamula kuti ndigule mundawo pali mboni ziŵiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ngakhale mzindawu udzaperekedwa kwa Ababuloni, komabe Inu Ambuye Yehova, munandiwuza kuti, ‘Gula munda ndi siliva ndipo upereke ndalamazo pali mboni.’ ” Onani mutuwo |