Yeremiya 32:22 - Buku Lopatulika22 ndipo munawapatsa iwo dziko ili, limene munalumbirira makolo ao kuti mudzawapatsa, dziko moyenda mkaka ndi uchi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 ndipo munawapatsa iwo dziko ili, limene munalumbirira makolo ao kuti mudzawapatsa, dziko moyenda mkaka ndi uchi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mudaŵapatsa dziko lino, limene mudalonjeza makolo ao molumbira, dziko lamwanaalirenji. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Munawapatsa dziko lino limene munalonjeza mwalumbiro kulipereka kwa makolo awo, dziko loyenda mkaka ndi uchi. Onani mutuwo |