Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 32:14 - Buku Lopatulika

14 Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero; Tenga makalata awa, kalata yogulira, yosindikizidwa, ndi kalata yovundukuka, nuwaike m'mbiya yadothi; kuti akhale masiku ambiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero; Tenga akalata awa, kalata uyu wogulira, wosindikizidwa, ndi kalata uyu wovundukuka, nuwaike m'mbiya yadothi; kuti akhale masiku ambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Chauta Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israele, walamula kuti iweyo utenge makalata a umboni wa chipanganoŵa, inai yomata inai yosamata, uŵasunge m'mbiya kuti akhale nthaŵi yaitali.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 ‘Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti: Tenga makalata awa a umboni wapangano, iyi yokhala ndi chizindikiro ndi yopanda chizindikiro, uwasunge mʼmbiya kuti akhale nthawi yayitali.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 32:14
3 Mawu Ofanana  

Atero Yehova, Pita, nugule nsupa ya woumba, nutenge akulu a anthu, ndi akulu a ansembe;


Ndipo ndinauza Baruki pamaso pao, kuti,


Pakuti Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero: Nyumba ndi minda ndi minda yampesa idzagulidwanso m'dziko muno.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa