Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 32:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo ndinauza Baruki pamaso pao, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo ndinauza Baruki pamaso pao, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ndidamlangiza Baruki pamaso pa onsewo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “Ndinamulangiza Baruki pamaso pa onsewo kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 32:13
2 Mawu Ofanana  

ndipo ndinapereka kalata yogulirayo kwa Baruki mwana wa Neriya, mwana wa Maseiya, pamaso pa Hanamele mwana wa mbale wa atate wanga, ndi pamaso pa mboni zimene zinalemba pa kalata yogulirayo, pamaso pa Ayuda onse okhala m'bwalo la kaidi.


Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero; Tenga makalata awa, kalata yogulira, yosindikizidwa, ndi kalata yovundukuka, nuwaike m'mbiya yadothi; kuti akhale masiku ambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa