Yeremiya 31:2 - Buku Lopatulika2 Atero Yehova, Anthu opulumuka m'lupanga anapeza chisomo m'chipululu; Israele, muja anakapuma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Atero Yehova, Anthu opulumuka m'lupanga anapeza chisomo m'chipululu; Israele, muja anakapuma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mau a Chauta ndi aŵa, “Anthu amene adapulumuka ku nkhondo, ndidaŵakomera mtima m'chipululu. Pamene Aisraele ankafuna kupumula, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova akuti, “Anthu amene anapulumuka ku nkhondo ndinawakomera mtima mʼchipululu; pamene Aisraeli ankafuna kupumula.” Onani mutuwo |