Yeremiya 30:9 - Buku Lopatulika9 koma adzamtumikira Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, imene Ndidzawaukitsira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 koma adzamtumikira Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, imene Ndidzawaukitsira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Azidzangotumikira Chauta, Mulungu wao, ndi Davide, mfumu yao, amene ndidzaŵasankhulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mʼmalo mwake, adzatumikira Yehova Mulungu wawo ndiponso Davide mfumu yawo, amene ndidzawasankhira. Onani mutuwo |