Yeremiya 30:7 - Buku Lopatulika7 Kalanga ine! Pakuti nlalikulu tsikulo, palibe lina lotere; ndi nthawi ya msauko wa Yakobo; koma adzapulumuka m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kalanga ine! Pakuti nlalikulu tsikulo, palibe lina lotere; ndi nthawi ya msauko wa Yakobo; koma adzapulumuka m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Kalanga ine! Tsiku limenelo nlalikulu kwambiri, sipadzakhala lina lofanana nalo. Idzakhala nthaŵi yamavuto kwa Yakobe, komabe adzapulumuka ku mavutowo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mayo ine! Tsiku limeneli ndi lalikulu kwambiri! Sipadzakhala lina lofanana nalo. Idzakhala nthawi ya masautso kwa Yakobo, koma adzapulumuka ku masautsowo.” Onani mutuwo |