Yeremiya 30:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti Yehova atero: Tamva ife mau akunthunthumira, ndi amantha, si amtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti Yehova atero: Tamva ife mau akunthunthumira, ndi amantha, si amtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Tamva kulira kwankhaŵa, kufuula kwamantha, ndipo palibe mtendere paliponse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Yehova akuti: “Ndamva kulira chifukwa cha nkhawa, ndamva kulira kwa mantha popeza palibe mtendere. Onani mutuwo |