Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 30:4 - Buku Lopatulika

4 Awa ndi mau ananena Yehova za Israele ndi Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Awa ndi mau ananena Yehova za Israele ndi Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mau amene akunena za Israele ndi Yuda ndi aŵa:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Nawa mawu amene Yehova anayankhula ndi anthu a ku Israeli ndi Yuda:

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 30:4
2 Mawu Ofanana  

Pakuti, taona, masiku adzadza, ati Yehova, amene ndidzabwezanso undende wa anthu anga Aisraele ndi Ayuda, ati Yehova; ndipo ndidzawabwezera kudziko limene ndinapatsa makolo ao. Ndipo adzakhala nalo.


Pakuti Yehova atero: Tamva ife mau akunthunthumira, ndi amantha, si amtendere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa