Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 30:23 - Buku Lopatulika

23 Taonani, chimphepo cha Yehova, kupsa mtima kwake, chatuluka, chimphepo chakukokolola: chidzagwa pamutu pa oipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Taonani, chimphepo cha Yehova, kupsa mtima kwake, chatuluka, chimphepo chakukokolola: chidzagwa pamtu pa oipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 “Onani, mphepo yamkuntho ya Chauta! Mkuntho wamphamvu wa kamvulumvulu, ukuwomba pa mitu ya anthu olakwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Taonani ukali wa Yehova wowomba ngati mphepo ya mkuntho. Mphepo ya namondwe ikuwomba pa mitu ya anthu oyipa.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 30:23
7 Mawu Ofanana  

Miphika yanu isanagwire moto waminga, adzaiuluza, yaiwisi ndi yoyaka.


pakudza mantha anu ngati mphepo yopasula, ndi pofika tsoka lanu ngati kamvulumvulu; pakudza kwa inu vuto ndi nsautso.


Yehova wa makamu atero, Taonani, zoipa zidzatuluka kumtundu kunka m'mitundu, ndipo namondwe adzauka kuchokera ku malekezero a dziko lapansi.


Pa nthawi yomweyo adzati kwa anthu awa ndi kwa Yerusalemu, Mphepo yotentha yochokera kumapiri oti see m'chipululu yopita kwa mwana wamkazi wa anthu anga, yosapetera, yosayeretsa;


Kodi muyesa chimenechi chabe, nonsenu opita panjira? Penyani nimuone, kodi chilipo chisoni china ngati changachi amandimvetsa ine, chimene Yehova wandisautsa nacho tsiku la mkwiyo wake waukali?


Ndipo Yehova adzaoneka pamwamba pao, ndi muvi wake udzatuluka ngati mphezi; ndipo Ambuye Mulungu adzaomba lipenga, nadzayenda ndi akamvulumvulu a kumwera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa