Yeremiya 30:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa chake iwo akulusira iwe adzalusiridwanso; ndi adani ako onse, adzanka ku undende onsewo; ndipo iwo adzakufunkha iwe adzakhala chofunkha, ndipo onse akulanda iwe ndidzapereka kuti zilandidwe zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa chake iwo akulusira iwe adzalusidwanso; ndi adani ako onse, adzanka ku undende onsewo; ndipo iwo adzakufunkha iwe adzakhala chofunkha, ndipo onse akulanda iwe ndidzapereka kuti zilandidwe zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono onse amene adakuwonongani inu, ndidzaŵaononga iwonso. Onse okuzunzani adzatengedwa ukapolo. Onse ofunkha zinthu zanu, nawonso zao zidzafunkhidwa. Ndipo onse okusakazani, ndidzachita zoti nawonso aŵasakaze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Tsono onse amene anakuwonongani, nawonso adzawonongedwa; adani anu onse adzapita ku ukapolo. Iwo amene anafunkha zinthu zanu, zinthu zawo zidzafunkhidwanso; onse amene anakusakazani nawonso adzasakazidwa. Onani mutuwo |