Yeremiya 30:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti atero Yehova, Kulaswa kwako kuli kosapoleka ndi bala lako lili lowawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti atero Yehova, Kulaswa kwako kuli kosapoleka ndi bala lako lili lowawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chauta akunena kuti, “Chilonda chanu nchosachizika, bala lanu nlonyeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yehova akuti, “Chilonda chanu nʼchosachizika, bala lanu ndi lonyeka. Onani mutuwo |