Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 30:1 - Buku Lopatulika

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Yeremiya kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anawuza Yeremiya kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 30:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo wokhala m'mphepete mwa nyanja muno adzati tsiku limenelo, Taonani, kuyembekeza kwathu kuli kotero, kumene ife tinathawira atithangate kupulumutsidwa kwa mfumu ya Asiriya, ndipo ife tidzapulumuka bwanji?


Koma mudziwe ndithu kuti, ngati mudzandipha ine, mudzadzitengera nokha mwazi wosachimwa, ndi pa mzinda uwu, ndi pa okhalamo ake; pakuti mwa ntheradi Yehova wandituma kwa inu kuti ndinene mau onse awa m'makutu anu.


chifukwa chake atero Yehova, Taonani, ndidzalanga Semaya Mnehelamu, ndi mbeu zake; sadzakhala ndi munthu wakukhala mwa anthu awa, sadzaona zabwino ndidzachitira anthu anga, ati Yehova: chifukwa wanena zopikisana ndi Yehova.


Atero Yehova, Mulungu wa Israele, kuti, Lemba m'buku mau onse amene ndanena kwa iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa