Yeremiya 3:21 - Buku Lopatulika21 Mau amveka pa mapiri oti see, kulira ndi kupempha kwa ana a Israele; pakuti anaipitsa njira yao, naiwala Yehova Mulungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Mau amveka pa mapiri oti see, kulira ndi kupempha kwa ana a Israele; pakuti anaipitsa njira yao, naiwala Yehova Mulungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Pakumveka liwu pa magomo, Aisraele akulira ndiponso akupempha chifundo, pakuti atsata njira zoipa, ndipo aiŵala Chauta, Mulungu wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mawu akumveka pa magomo, Aisraeli akulira ndi kupempha chifundo chifukwa anatsata njira zoyipa ndi kuyiwala Yehova Mulungu wawo. Onani mutuwo |