Yeremiya 3:20 - Buku Lopatulika20 Ndithu monga mkazi achokera mwamuna wake monyenga, chomwecho mwachita ndi Ine monyenga, inu nyumba ya Israele, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndithu monga mkazi achokera mwamuna wake monyenga, chomwecho mwachita ndi Ine monyenga, inu nyumba ya Israele, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ndithu, monga momwe mkazi wosakhulupirika amasiyira mwamuna wake, iwenso Israele wakhala wosakhulupirika kwa Ine,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma monga mkazi wosakhulupirika amasiya mwamuna wake, momwemonso inu mwakhala osakhulupirika kwa Ine, inu fuko la Israeli,” akutero Yehova. Onani mutuwo |