Yeremiya 3:18 - Buku Lopatulika18 Masiku omwewo nyumba ya Yuda idzayenderena ndi nyumba ya Israele, ndipo adzatuluka pamodzi kudziko la kumpoto kunka ku dziko limene ndinapatsa makolo anu kuti alowemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Masiku omwewo nyumba ya Yuda idzayenderena ndi nyumba ya Israele, ndipo adzatuluka pamodzi kudziko la kumpoto kunka ku dziko limene ndinapatsa makolo anu kuti alowemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Masiku amenewo fuko la Yuda lidzaphathana ndi fuko la Israele. Onse pamodzi adzachokera ku dziko lakumpoto kupita ku dziko limene ndidapatsa makolo ao, kuti likhale choloŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Masiku amenewo fuko la Yuda lidzaphatikizana ndi fuko la Israeli, onse pamodzi adzachokera ku dziko la kumpoto kupita ku dziko limene ndinapatsa makolo awo, kuti likhale cholowa. Onani mutuwo |