Yeremiya 3:14 - Buku Lopatulika14 Bwerani, ananu obwerera, ati Yehova; pakuti Ine ndine mbuye wanu; ndipo ndidzakutengani inu mmodzimmodzi wa pa mzinda uliwonse, ndi awiriawiri a pa banja lililonse, ndi kukutengerani ku Ziyoni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Bwerani, ananu obwerera, ati Yehova; pakuti Ine ndine mbuye wanu; ndipo ndidzakutengani inu mmodzimmodzi wa pa mudzi uliwonse, ndi awiriawiri a pa banja lililonse, ndi kukutengerani ku Ziyoni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Bwererani inu anthu osakhulupirika, pakuti mbuye wanu ndine. Ndidzakutengani kupita nanu ku Ziyoni, mmodzi kuchokera ku mzinda uliwonse, aŵiri kuchokera ku banja lililonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Bwererani, ana osakhulupirika, pakuti ndine mbuye wanu,” akutero Yehova. “Ndinakusankhani, mmodzimmodzi kuchokera ku mudzi uliwonse ndiponso awiriawiri kuchokera ku banja lililonse. Onani mutuwo |