Yeremiya 28:9 - Buku Lopatulika9 Mneneri amene anenera za mtendere, pamene mau a mneneri adzachitidwa, pamenepo mneneri adzadziwika, kuti Yehova anamtuma ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mneneri amene anenera za mtendere, pamene mau a mneneri adzachitidwa, pamenepo mneneri adzadziwika, kuti Yehova anamtuma ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma ngati mneneri alosa za mtendere, zimene walosazo zikachitikadi, pamenepo zidzadziŵika kuti Chauta adamtumadi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma mneneri amene amalosera zamtendere adzadziwika kuti ndi woona ndi kuti watumidwa ndi Yehova ngati zimene wanenera zachitikadi.” Onani mutuwo |