Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 28:8 - Buku Lopatulika

8 Aneneri amene analipo kale ndisanakhale ine, nimusanakhale inu, ananenera maiko ambiri, ndi mafumu aakulu, za nkhondo, ndi za choipa, ndi za mliri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Aneneri amene analipo kale ndisanakhale ine, nimusanakhale inu, ananenera maiko ambiri, ndi mafumu akulu, za nkhondo, ndi za choipa, ndi za chaola.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Aneneri amene adatsogola kale ankalosa za nkhondo, za njala ndi za mliri, zodzagwera maiko ambiri ndi maufumu otchuka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Kunali aneneri kalelo, ine ndi iwe tisanabadwe. Iwowa analosera za nkhondo, mavuto ndi mliri kuti zidzagwera mayiko ambiri ndi maufumu amphamvu.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 28:8
25 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya wa ku Tisibe wokhala ku Giliyadi ananena ndi Ahabu, nati, Pali Yehova Mulungu wa Israele, amene ndimakhala pamaso pake, ngati adzagwa mame kapena mvula zaka izi, koma ntanena ine ndipo.


Nati iye, Ndinaona Aisraele onse obalalika pamapiri ngati nkhosa zopanda mbusa; ndipo Yehova anati, Izi zilibe mwini, yense abwerere ndi mtendere kunyumba yake.


Ndipo mfumu ya Israele inati kwa Yehosafati, Alipo munthu wina kuti tifunsire kwa Yehova mwa iye; koma ndimuda, popeza samanenera za ine zabwino, koma zoipa; ndiye Mikaya mwana wake wa Imila. Nati Yehosafati, Isamatero mfumu.


Katundu wa Babiloni, amene anamuona Yesaya mwana wa Amozi.


Mauta ao adzatha anyamata; ndipo sadzachitira chisoni chipatso cha mimba; diso lao silidzaleka ana.


Mau a Amosi, amene anali mwa oweta ng'ombe a ku Tekowa, ndiwo amene anawaona za Israele masiku a Uziya mfumu ya Yuda, ndi masiku a Yerobowamu mwana wa Yowasi mfumu ya Israele, zitatsala zaka ziwiri chisanafike chivomezi.


Ndipo anati, Yehova adzadzuma ali mu Ziyoni, nadzamveketsa mau ake ali mu Yerusalemu; podyetsa abusa padzachita chisoni, ndi mutu wa Karimele udzauma.


Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona nthawi yachiwiri, ndi kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa